Add parallel Print Page Options

Paulo, Silivano ndi Timoteyo.

Tikulembera mpingo wa ku Tesalonika, umene uli mwa Mulungu Atate ndi Ambuye Yesu Khristu.

Chisomo ndi mtendere kwa inu.

Kuyamikira Chikhulupiriro cha Atesalonika

Ife timayamika Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu. Timakutchulani mʼmapemphero athu. Nthawi zonse timakumbukira ntchito yanu yachikhulupiriro, yachikondi ndi kupirira kwanu kwa chiyembekezo mwa Ambuye athu Yesu Khristu, pamaso pa Mulungu wathu ndi Atate.

Abale okondedwa ndi Mulungu, tikudziwa kuti Mulungu anakusankhani, chifukwa uthenga wathu wabwino sunafike kwa inu ndi mawu okha, koma ndi mphamvu za Mzimu Woyera ndi chitsimikizo chachikulu. Mukudziwa mmene tinkakhalira pakati panu kuti tikuthandizeni. Inu mwakhala otitsatira athu ndi a Ambuye; ngakhale kuti panali masautso akulu, munalandira uthenga mwachimwemwe chochokera kwa Mzimu Woyera. Ndipo potero munakhala chitsanzo kwa abale onse a ku Makedoniya ndi Akaya. Kuchokera kwa inu, uthenga wa Ambuye unamveka ku Makedoniya ndi ku Akaya ndipo mbiri ya chikhulupiriro chanu mwa Mulungu yamveka ponseponse. Choncho sikofunikanso kuti tinene kanthu, pakuti iwo amafotokoza za momwe munatilandirira. Iwo amatiwuza za momwe munatembenukira kwa Mulungu kusiya mafano ndi kutumikira Mulungu wamoyo ndi woona. 10 Ndipo mukudikira Mwana wake kuchokera kumwamba, Yesu, amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa. Iyeyo amatipulumutsa ku mkwiyo umene ukubwera.

Paul, Silas[a](A) and Timothy,(B)

To the church of the Thessalonians(C) in God the Father and the Lord Jesus Christ:

Grace and peace to you.(D)

Thanksgiving for the Thessalonians’ Faith

We always thank God for all of you(E) and continually mention you in our prayers.(F) We remember before our God and Father(G) your work produced by faith,(H) your labor prompted by love,(I) and your endurance inspired by hope(J) in our Lord Jesus Christ.

For we know, brothers and sisters[b] loved by God,(K) that he has chosen you, because our gospel(L) came to you not simply with words but also with power,(M) with the Holy Spirit and deep conviction. You know(N) how we lived among you for your sake. You became imitators of us(O) and of the Lord, for you welcomed the message in the midst of severe suffering(P) with the joy(Q) given by the Holy Spirit.(R) And so you became a model(S) to all the believers in Macedonia(T) and Achaia.(U) The Lord’s message(V) rang out from you not only in Macedonia and Achaia—your faith in God has become known everywhere.(W) Therefore we do not need to say anything about it, for they themselves report what kind of reception you gave us. They tell how you turned(X) to God from idols(Y) to serve the living and true God,(Z) 10 and to wait for his Son from heaven,(AA) whom he raised from the dead(AB)—Jesus, who rescues us from the coming wrath.(AC)

Footnotes

  1. 1 Thessalonians 1:1 Greek Silvanus, a variant of Silas
  2. 1 Thessalonians 1:4 The Greek word for brothers and sisters (adelphoi) refers here to believers, both men and women, as part of God’s family; also in 2:1, 9, 14, 17; 3:7; 4:1, 10, 13; 5:1, 4, 12, 14, 25, 27.