Add parallel Print Page Options

Mbiri ya Makolo Kuchokera pa Adamu Mpaka pa Abrahamu

Mpaka pa Ana a Nowa

Adamu, Seti, Enosi Kenani, Mahalaleli, Yaredi, Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.

Ana a Nowa,

Semu, Hamu ndi Yafeti.

Fuko la Yafeti

Ana aamuna a Yafeti anali:

Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.

Ana aamuna a Gomeri anali:

Asikenazi, Rifati ndi Togarima

Ana aamuna a Yavani anali:

Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.

Fuko la Hamu

Ana aamuna a Hamu anali:

Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani

Ana aamuna a Kusi anali:

Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka

Ana aamuna a Raama anali:

Seba ndi Dedani.

10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu

kwambiri pa dziko lapansi.

11 Igupto ndiye kholo la

Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu, 12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.

13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni,

ndipo anaberekanso Ahiti, 14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi 15 Ahivi, Aariki, Asini 16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.

Fuko la Semu

17 Ana aamuna a Semu anali:

Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu.

Ana aamuna a Aramu anali:

Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.

18 Aripakisadi anabereka Sela

ndipo Selayo anabereka Eberi:

19 Eberi anabereka ana aamuna awiri:

wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.

20 Yokitani anabereka

Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera, 21 Hadoramu, Uzali, Dikila 22 Obali, Abimaeli, Seba, 23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.

24 Semu, Aripakisadi, Sela

25 Eberi, Pelegi, Reu

26 Serugi, Nahori, Tera

27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).

Banja la Abrahamu

28 Ana a Abrahamu ndi awa:

Isake ndi Ismaeli.

Zidzukulu za Hagara

29 Zidzukulu zake zinali izi:

Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu, 30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema, 31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.

Zidzukulu za Ketura

32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa:

Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa.

Ana a Yokisani ndi awa:

Seba ndi Dedani

33 Ana aamuna a Midiyani anali,

Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida.

Onsewa anali zidzukulu za Ketura.

Zidzukulu za Sara

34 Abrahamu anabereka Isake.

Ana a Isake anali awa:

Esau ndi Israeli.

Ana a Esau

35 Ana aamuna a Esau anali awa:

Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.

36 Ana a Elifazi anali awa:

Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi:

Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.

37 Ana a Reueli anali awa:

Nahati, Zera, Sama ndi Miza.

Anthu a ku Seiri ku Edomu

38 Ana a Seiri anali awa:

Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.

39 Ana aamuna a Lotani anali awa:

Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.

40 Ana aamuna a Sobala anali awa:

Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu.

Ana aamuna a Zibeoni anali awa:

Ayiwa ndi Ana.

41 Mwana wa Ana anali

Disoni.

Ana a Disoni anali awa:

Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani

42 Ana aamuna a Ezeri anali awa:

Bilihani, Zaavani ndi Yaakani.

Ana aamuna a Disani anali awa:

Uzi ndi Arani.

Mafumu a ku Edomu

43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko:

Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.

44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.

45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.

46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.

47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.

48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.

49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.

50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu. 51 Hadadi anamwaliranso.

Mafumu a ku Edomu anali:

Timna, Aliva, Yeteti, 52 Oholibama, Ela, Pinoni, 53 Kenazi, Temani, Mibezari, 54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

Historical Records From Adam to Abraham

To Noah’s Sons

Adam,(A) Seth, Enosh, Kenan,(B) Mahalalel,(C) Jared,(D) Enoch,(E) Methuselah,(F) Lamech,(G) Noah.(H)

The sons of Noah:[a](I)

Shem, Ham and Japheth.(J)

The Japhethites(K)

The sons[b] of Japheth:

Gomer, Magog, Madai, Javan, Tubal, Meshek and Tiras.

The sons of Gomer:

Ashkenaz, Riphath[c] and Togarmah.

The sons of Javan:

Elishah, Tarshish, the Kittites and the Rodanites.

The Hamites(L)

The sons of Ham:

Cush, Egypt, Put and Canaan.

The sons of Cush:

Seba, Havilah, Sabta, Raamah and Sabteka.

The sons of Raamah:

Sheba and Dedan.

10 Cush was the father[d] of

Nimrod, who became a mighty warrior on earth.

11 Egypt was the father of

the Ludites, Anamites, Lehabites, Naphtuhites, 12 Pathrusites, Kasluhites (from whom the Philistines came) and Caphtorites.

13 Canaan was the father of

Sidon his firstborn,[e] and of the Hittites, 14 Jebusites, Amorites, Girgashites, 15 Hivites, Arkites, Sinites, 16 Arvadites, Zemarites and Hamathites.

The Semites(M)

17 The sons of Shem:

Elam, Ashur, Arphaxad, Lud and Aram.

The sons of Aram:[f]

Uz, Hul, Gether and Meshek.

18 Arphaxad was the father of Shelah,

and Shelah the father of Eber.

19 Two sons were born to Eber:

One was named Peleg,[g] because in his time the earth was divided; his brother was named Joktan.

20 Joktan was the father of

Almodad, Sheleph, Hazarmaveth, Jerah, 21 Hadoram, Uzal, Diklah, 22 Obal,[h] Abimael, Sheba, 23 Ophir, Havilah and Jobab. All these were sons of Joktan.

24 Shem,(N) Arphaxad,[i] Shelah,

25 Eber, Peleg, Reu,

26 Serug, Nahor, Terah

27 and Abram (that is, Abraham).

The Family of Abraham

28 The sons of Abraham:

Isaac and Ishmael.

Descendants of Hagar(O)

29 These were their descendants:

Nebaioth the firstborn of Ishmael, Kedar, Adbeel, Mibsam, 30 Mishma, Dumah, Massa, Hadad, Tema, 31 Jetur, Naphish and Kedemah. These were the sons of Ishmael.

Descendants of Keturah(P)

32 The sons born to Keturah, Abraham’s concubine:(Q)

Zimran, Jokshan, Medan, Midian, Ishbak and Shuah.

The sons of Jokshan:

Sheba and Dedan.(R)

33 The sons of Midian:

Ephah, Epher, Hanok, Abida and Eldaah.

All these were descendants of Keturah.

Descendants of Sarah(S)

34 Abraham(T) was the father of Isaac.(U)

The sons of Isaac:

Esau and Israel.(V)

Esau’s Sons

35 The sons of Esau:(W)

Eliphaz, Reuel,(X) Jeush, Jalam and Korah.

36 The sons of Eliphaz:

Teman, Omar, Zepho,[j] Gatam and Kenaz;

by Timna: Amalek.[k](Y)

37 The sons of Reuel:(Z)

Nahath, Zerah, Shammah and Mizzah.

The People of Seir in Edom(AA)

38 The sons of Seir:

Lotan, Shobal, Zibeon, Anah, Dishon, Ezer and Dishan.

39 The sons of Lotan:

Hori and Homam. Timna was Lotan’s sister.

40 The sons of Shobal:

Alvan,[l] Manahath, Ebal, Shepho and Onam.

The sons of Zibeon:

Aiah and Anah.(AB)

41 The son of Anah:

Dishon.

The sons of Dishon:

Hemdan,[m] Eshban, Ithran and Keran.

42 The sons of Ezer:

Bilhan, Zaavan and Akan.[n]

The sons of Dishan[o]:

Uz and Aran.

The Rulers of Edom(AC)

43 These were the kings who reigned in Edom before any Israelite king reigned:

Bela son of Beor, whose city was named Dinhabah.

44 When Bela died, Jobab son of Zerah from Bozrah succeeded him as king.

45 When Jobab died, Husham from the land of the Temanites(AD) succeeded him as king.

46 When Husham died, Hadad son of Bedad, who defeated Midian in the country of Moab, succeeded him as king. His city was named Avith.

47 When Hadad died, Samlah from Masrekah succeeded him as king.

48 When Samlah died, Shaul from Rehoboth on the river[p] succeeded him as king.

49 When Shaul died, Baal-Hanan son of Akbor succeeded him as king.

50 When Baal-Hanan died, Hadad succeeded him as king. His city was named Pau,[q] and his wife’s name was Mehetabel daughter of Matred, the daughter of Me-Zahab. 51 Hadad also died.

The chiefs of Edom were:

Timna, Alvah, Jetheth, 52 Oholibamah, Elah, Pinon, 53 Kenaz, Teman, Mibzar, 54 Magdiel and Iram. These were the chiefs of Edom.

Footnotes

  1. 1 Chronicles 1:4 Septuagint; Hebrew does not have this line.
  2. 1 Chronicles 1:5 Sons may mean descendants or successors or nations; also in verses 6-9, 17 and 23.
  3. 1 Chronicles 1:6 Many Hebrew manuscripts and Vulgate (see also Septuagint and Gen. 10:3); most Hebrew manuscripts Diphath
  4. 1 Chronicles 1:10 Father may mean ancestor or predecessor or founder; also in verses 11, 13, 18 and 20.
  5. 1 Chronicles 1:13 Or of the Sidonians, the foremost
  6. 1 Chronicles 1:17 One Hebrew manuscript and some Septuagint manuscripts (see also Gen. 10:23); most Hebrew manuscripts do not have this line.
  7. 1 Chronicles 1:19 Peleg means division.
  8. 1 Chronicles 1:22 Some Hebrew manuscripts and Syriac (see also Gen. 10:28); most Hebrew manuscripts Ebal
  9. 1 Chronicles 1:24 Hebrew; some Septuagint manuscripts Arphaxad, Cainan (see also note at Gen. 11:10)
  10. 1 Chronicles 1:36 Many Hebrew manuscripts, some Septuagint manuscripts and Syriac (see also Gen. 36:11); most Hebrew manuscripts Zephi
  11. 1 Chronicles 1:36 Some Septuagint manuscripts (see also Gen. 36:12); Hebrew Gatam, Kenaz, Timna and Amalek
  12. 1 Chronicles 1:40 Many Hebrew manuscripts and some Septuagint manuscripts (see also Gen. 36:23); most Hebrew manuscripts Alian
  13. 1 Chronicles 1:41 Many Hebrew manuscripts and some Septuagint manuscripts (see also Gen. 36:26); most Hebrew manuscripts Hamran
  14. 1 Chronicles 1:42 Many Hebrew and Septuagint manuscripts (see also Gen. 36:27); most Hebrew manuscripts Zaavan, Jaakan
  15. 1 Chronicles 1:42 See Gen. 36:28; Hebrew Dishon, a variant of Dishan
  16. 1 Chronicles 1:48 Possibly the Euphrates
  17. 1 Chronicles 1:50 Many Hebrew manuscripts, some Septuagint manuscripts, Vulgate and Syriac (see also Gen. 36:39); most Hebrew manuscripts Pai