Add parallel Print Page Options

Chionetsero cha Kuzingidwa kwa Yerusalemu

Mulungu anati, “Iwe mwana wa munthu, tsopano tenga njerwa, uliyike pamaso pako ndipo ujambulepo chithunzi cha mzinda wa Yerusalemu. Ndipo uwuzinge mzindawo motere: uwumangire nsanja zowuzinga, uwumbire mitumbira ya nkhondo, uwumangire misasa ya nkhondo ndipo uyike zida zogumulira kuzungulira mzindawo. Kenaka utenge chiwaya chachitsulo uchiyike ngati khoma lachitsulo pakati pa iwe ndi mzindawo. Uyangʼanitsitse mzindawo ndipo udzakhala wozingidwa ndi nsanja za nkhondo. Choncho umangire nsanja zankhondo. Chimenechi chidzakhala chizindikiro kwa Aisraeli.

“Tsono iwe ugonere kumanzere kwako ndipo ndidzayika pa iwe tchimo la Aisraeli. Iwe udzasenza tchimolo masiku onse amene udzagonere mbali imeneyo. Ine ndakuyikira masiku okwana 390 malingana ndi zaka za machimo awo. Umu ndi mmene udzasenzere machimo a Aisraeli.

“Utatha zimenezo udzagonerenso mbali ya kudzanja lamanja, ndipo udzasenza machimo a anthu a ku Yuda masiku makumi anayi, tsiku lililonse kuyimira chaka chimodzi. Tsono udzayangʼanitsitse nsanja za nkhondo zozinga. Dzanja la mkanjo wako utalikwinya ndi dzanja lako utakweza, udzalosere modzudzula Yerusalemu. Ine ndidzakumanga ndi zingwe kotero kuti sudzatha kutembenukira uku ndi uku mpaka utatsiriza masiku akuzingidwa ako.

“Tsono tenga tirigu ndi barele, nyemba ndi mphodza, mapira ndi mchewere; ndipo uyike zonsezi mʼmbale imodzi ndipo upange buledi wako. Uzidya pa masiku 390 amene udzakhala ukugonera mbali imodzi. 10 Uyeze theka la kilogalamu la chakudyacho kuti uzidya tsiku lililonse kamodzi kokha. 11 Uyezenso zikho ziwiri zamadzi ndipo uzimwa tsiku ndi tsiku. 12 Uzidya chakudya chako ngati momwe amadyera keke ya barele. Uzidzaphika chakudyacho anthu akuona pogwiritsa ntchito ndowe ya munthu ngati nkhuni.” 13 Yehova anati, “Chimodzimodzi anthu a Israeli adzadya chakudya chodetsedwa ku mayiko achilendo kumene Ine ndidzawapirikitsira.”

14 Koma ine ndinati, “Zisatero, Ambuye Yehova! Ine sindinadziyipitsepo pa zachipembedzo. Kuyambira ubwana wanga mpaka tsopano, sindinadyepo kanthu kalikonse kopezeka katafa kapena kophedwa ndi zirombo za kutchire. Palibe nyama yodetsedwa pa zachipembedzo imene inalowa pakamwa panga.”

15 Iye anati, “Chabwino, ndidzakulola kuti uphike buledi wako ndi ndowe za ngʼombe mʼmalo mwa ndowe za munthu.”

16 Pambuyo pake anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, anthu a ku Yerusalemu ndidzawachepetsera chakudya. Anthuwo adzadya chakudya chochita kuyeza ndipo azidzadya mwa nkhawa. Azidzamwanso madzi ochita kuyeza ndiponso mwa mantha. 17 Ndidzachita zimenezi kuti adzasowe chakudya ndi madzi. Choncho adzachita nkhawa akumapenyana ndipo adzatheratu ndi kuwonda chifukwa cha machimo awo.”

Siege of Jerusalem Symbolized

“Now, son of man, take a block of clay, put it in front of you and draw the city of Jerusalem on it. Then lay siege to it: Erect siege works against it, build a ramp(A) up to it, set up camps against it and put battering rams around it.(B) Then take an iron pan,(C) place it as an iron wall between you and the city and turn your face toward(D) it. It will be under siege, and you shall besiege it. This will be a sign(E) to the people of Israel.(F)

“Then lie on your left side and put the sin of the people of Israel upon yourself.[a] You are to bear their sin for the number of days you lie on your side. I have assigned you the same number of days as the years of their sin. So for 390 days you will bear the sin of the people of Israel.

“After you have finished this, lie down again, this time on your right side, and bear the sin(G) of the people of Judah. I have assigned you 40 days, a day for each year.(H) Turn your face(I) toward the siege of Jerusalem and with bared arm prophesy against her. I will tie you up with ropes so that you cannot turn from one side to the other until you have finished the days of your siege.(J)

“Take wheat and barley, beans and lentils, millet and spelt;(K) put them in a storage jar and use them to make bread for yourself. You are to eat it during the 390 days you lie on your side. 10 Weigh out twenty shekels[b](L) of food to eat each day and eat it at set times. 11 Also measure out a sixth of a hin[c] of water and drink it at set times.(M) 12 Eat the food as you would a loaf of barley bread; bake it in the sight of the people, using human excrement(N) for fuel.” 13 The Lord said, “In this way the people of Israel will eat defiled food among the nations where I will drive them.”(O)

14 Then I said, “Not so, Sovereign Lord!(P) I have never defiled myself. From my youth until now I have never eaten anything found dead(Q) or torn by wild animals. No impure meat has ever entered my mouth.(R)

15 “Very well,” he said, “I will let you bake your bread over cow dung instead of human excrement.”

16 He then said to me: “Son of man, I am about to cut off(S) the food supply in Jerusalem. The people will eat rationed food in anxiety and drink rationed water in despair,(T) 17 for food and water will be scarce.(U) They will be appalled at the sight of each other and will waste away because of[d] their sin.(V)

Footnotes

  1. Ezekiel 4:4 Or upon your side
  2. Ezekiel 4:10 That is, about 8 ounces or about 230 grams
  3. Ezekiel 4:11 That is, about 2/3 quart or about 0.6 liter
  4. Ezekiel 4:17 Or away in

Thou also, son of man, take thee a tile, and lay it before thee, and pourtray upon it the city, even Jerusalem:

And lay siege against it, and build a fort against it, and cast a mount against it; set the camp also against it, and set battering rams against it round about.

Moreover take thou unto thee an iron pan, and set it for a wall of iron between thee and the city: and set thy face against it, and it shall be besieged, and thou shalt lay siege against it. This shall be a sign to the house of Israel.

Lie thou also upon thy left side, and lay the iniquity of the house of Israel upon it: according to the number of the days that thou shalt lie upon it thou shalt bear their iniquity.

For I have laid upon thee the years of their iniquity, according to the number of the days, three hundred and ninety days: so shalt thou bear the iniquity of the house of Israel.

And when thou hast accomplished them, lie again on thy right side, and thou shalt bear the iniquity of the house of Judah forty days: I have appointed thee each day for a year.

Therefore thou shalt set thy face toward the siege of Jerusalem, and thine arm shall be uncovered, and thou shalt prophesy against it.

And, behold, I will lay bands upon thee, and thou shalt not turn thee from one side to another, till thou hast ended the days of thy siege.

Take thou also unto thee wheat, and barley, and beans, and lentiles, and millet, and fitches, and put them in one vessel, and make thee bread thereof, according to the number of the days that thou shalt lie upon thy side, three hundred and ninety days shalt thou eat thereof.

10 And thy meat which thou shalt eat shall be by weight, twenty shekels a day: from time to time shalt thou eat it.

11 Thou shalt drink also water by measure, the sixth part of an hin: from time to time shalt thou drink.

12 And thou shalt eat it as barley cakes, and thou shalt bake it with dung that cometh out of man, in their sight.

13 And the Lord said, Even thus shall the children of Israel eat their defiled bread among the Gentiles, whither I will drive them.

14 Then said I, Ah Lord God! behold, my soul hath not been polluted: for from my youth up even till now have I not eaten of that which dieth of itself, or is torn in pieces; neither came there abominable flesh into my mouth.

15 Then he said unto me, Lo, I have given thee cow's dung for man's dung, and thou shalt prepare thy bread therewith.

16 Moreover he said unto me, Son of man, behold, I will break the staff of bread in Jerusalem: and they shall eat bread by weight, and with care; and they shall drink water by measure, and with astonishment:

17 That they may want bread and water, and be astonied one with another, and consume away for their iniquity.