Add parallel Print Page Options

Kusalapa kwa Israeli

“Bwerani, tiyeni tibwerere kwa Yehova.
Iye watikhadzula,
    koma adzatichiritsa.
Iye wativulaza,
    koma adzamanga mabala athu.
Pakapita masiku awiri adzatitsitsimutsa;
    pa tsiku lachitatu Iye adzatiukitsa
    kuti tikhale ndi moyo pamaso pake.
Tiyeni timudziwe Yehova,
    tiyeni tilimbike kumudziwa Iye.
Adzabwera kwa ife mosakayikira konse
    ngati kutuluka kwa dzuwa;
adzabwera kwa ife ngati mvula ya mʼchilimwe,
    ngati mvula ya nthawi yamphukira imene imakhathamiritsa nthaka.”

Iwe Efereimu, kodi ndichite nawe chiyani?
    Kodi ndichite nawe chiyani, iwe Yuda?
Chikondi chanu chili ngati nkhungu yammawa,
    ngati mame a mmamawa amene amakamuka msanga.
Choncho ndakuwazani ngati nkhuni kudzera mwa aneneri anga,
    ndakuphani ndi mawu a pakamwa panga;
    chigamulo changa chinangʼanima ngati mphenzi pa inu.
Pakuti Ine ndimafuna chifundo osati nsembe,
    ndi kudziwa Mulungu kulekana ndi nsembe zopsereza.
Monga Adamu, anthuwa aphwanya pangano langa,
    iwo sanakhulupirike kwa Ine.
Giliyadi ndi mzinda wa anthu ochita zoyipa,
    okhala ndi zizindikiro za kuphana.
Monga momwe mbala zimadikirira anthu,
    magulu a ansembe amachitanso motero;
iwo amapha anthu pa njira yopita ku Sekemu,
    kupalamula milandu yochititsa manyazi.
10 Ndaona chinthu choopsa kwambiri
    mʼnyumba ya Israeli.
Kumeneko Efereimu akuchita zachiwerewere,
    ndipo Israeli wadzidetsa.

11 “Kunenanso za iwe Yuda,
    udzakolola chilango.

“Pamene ndiwabwezere anthu anga zinthu zabwino.”

Israel Unrepentant

“Come, let us return(A) to the Lord.
He has torn us to pieces(B)
    but he will heal us;(C)
he has injured us
    but he will bind up our wounds.(D)
After two days he will revive us;(E)
    on the third day(F) he will restore(G) us,
    that we may live in his presence.
Let us acknowledge the Lord;
    let us press on to acknowledge him.
As surely as the sun rises,
    he will appear;
he will come to us like the winter rains,(H)
    like the spring rains that water the earth.(I)

“What can I do with you, Ephraim?(J)
    What can I do with you, Judah?
Your love is like the morning mist,
    like the early dew that disappears.(K)
Therefore I cut you in pieces with my prophets,
    I killed you with the words of my mouth(L)
    then my judgments go forth like the sun.[a](M)
For I desire mercy, not sacrifice,(N)
    and acknowledgment(O) of God rather than burnt offerings.(P)
As at Adam,[b] they have broken the covenant;(Q)
    they were unfaithful(R) to me there.
Gilead is a city of evildoers,(S)
    stained with footprints of blood.
As marauders lie in ambush for a victim,(T)
    so do bands of priests;
they murder(U) on the road to Shechem,
    carrying out their wicked schemes.(V)
10 I have seen a horrible(W) thing in Israel:
    There Ephraim is given to prostitution,
    Israel is defiled.(X)

11 “Also for you, Judah,
    a harvest(Y) is appointed.

“Whenever I would restore the fortunes(Z) of my people,

Footnotes

  1. Hosea 6:5 The meaning of the Hebrew for this line is uncertain.
  2. Hosea 6:7 Or Like Adam; or Like human beings

Come, and let us return unto the Lord: for he hath torn, and he will heal us; he hath smitten, and he will bind us up.

After two days will he revive us: in the third day he will raise us up, and we shall live in his sight.

Then shall we know, if we follow on to know the Lord: his going forth is prepared as the morning; and he shall come unto us as the rain, as the latter and former rain unto the earth.

O Ephraim, what shall I do unto thee? O Judah, what shall I do unto thee? for your goodness is as a morning cloud, and as the early dew it goeth away.

Therefore have I hewed them by the prophets; I have slain them by the words of my mouth: and thy judgments are as the light that goeth forth.

For I desired mercy, and not sacrifice; and the knowledge of God more than burnt offerings.

But they like men have transgressed the covenant: there have they dealt treacherously against me.

Gilead is a city of them that work iniquity, and is polluted with blood.

And as troops of robbers wait for a man, so the company of priests murder in the way by consent: for they commit lewdness.

10 I have seen an horrible thing in the house of Israel: there is the whoredom of Ephraim, Israel is defiled.

11 Also, O Judah, he hath set an harvest for thee, when I returned the captivity of my people.