Add parallel Print Page Options

136 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Yamikani Mulungu wa milungu.
Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Yamikani Ambuye wa ambuye,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Dzuwa lilamulire usana,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

10 Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
11 Natulutsa Israeli pakati pawo,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
12 Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

13 Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
14 Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
15 Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

16 Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
17 Amene anakantha mafumu akuluakulu,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
18 Napha mafumu amphamvu,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
19 Siloni mfumu ya Aamori,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
20 Ogi mfumu ya Basani,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
21 Napereka dziko lawo ngati cholowa,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
22 Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

23 Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
24 Amene anatimasula kwa adani athu,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.
25 Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

26 Yamikani Mulungu wakumwamba,
pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

Psalm 136

Give thanks(A) to the Lord, for he is good.(B)
His love endures forever.(C)
Give thanks(D) to the God of gods.(E)
His love endures forever.
Give thanks(F) to the Lord of lords:(G)
His love endures forever.

to him who alone does great wonders,(H)
His love endures forever.
who by his understanding(I) made the heavens,(J)
His love endures forever.
who spread out the earth(K) upon the waters,(L)
His love endures forever.
who made the great lights(M)
His love endures forever.
the sun to govern(N) the day,
His love endures forever.
the moon and stars to govern the night;
His love endures forever.

10 to him who struck down the firstborn(O) of Egypt
His love endures forever.
11 and brought Israel out(P) from among them
His love endures forever.
12 with a mighty hand(Q) and outstretched arm;(R)
His love endures forever.

13 to him who divided the Red Sea[a](S) asunder
His love endures forever.
14 and brought Israel through(T) the midst of it,
His love endures forever.
15 but swept Pharaoh and his army into the Red Sea;(U)
His love endures forever.

16 to him who led his people through the wilderness;(V)
His love endures forever.

17 to him who struck down great kings,(W)
His love endures forever.
18 and killed mighty kings(X)
His love endures forever.
19 Sihon king of the Amorites(Y)
His love endures forever.
20 and Og king of Bashan(Z)
His love endures forever.
21 and gave their land(AA) as an inheritance,(AB)
His love endures forever.
22 an inheritance(AC) to his servant Israel.(AD)
His love endures forever.

23 He remembered us(AE) in our low estate
His love endures forever.
24 and freed us(AF) from our enemies.(AG)
His love endures forever.
25 He gives food(AH) to every creature.
His love endures forever.

26 Give thanks(AI) to the God of heaven.(AJ)
His love endures forever.(AK)

Footnotes

  1. Psalm 136:13 Or the Sea of Reeds; also in verse 15