Add parallel Print Page Options

150 Tamandani Yehova.

Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika;
    mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu;
    mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
Mutamandeni poyimba malipenga,
    mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,
    mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga,
    mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.

Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.

Tamandani Yehova.

Psalm 150

Praise the Lord.[a](A)

Praise God in his sanctuary;(B)
    praise him in his mighty heavens.(C)
Praise him for his acts of power;(D)
    praise him for his surpassing greatness.(E)
Praise him with the sounding of the trumpet,(F)
    praise him with the harp and lyre,(G)
praise him with timbrel and dancing,(H)
    praise him with the strings(I) and pipe,(J)
praise him with the clash of cymbals,(K)
    praise him with resounding cymbals.

Let everything(L) that has breath praise the Lord.

Praise the Lord.

Footnotes

  1. Psalm 150:1 Hebrew Hallelu Yah; also in verse 6