Add parallel Print Page Options

91 Iye amene amakhala mu mthunzi wa Wammwambamwamba
    adzapuma mu mthunzi wa Wamphamvuzonse.
Ndidzanena za Yehova, “Iye ndiye pothawira panga ndi linga langa,
    Mulungu wanga amene ndimadalira.”

Ndithu, Iye adzakupulumutsa ku msampha wa mlenje
    ndi ku mliri woopsa;
Adzakuphimba ndi nthenga zake,
    ndipo udzapeza malo othawira mʼmapikomo;
    kukhulupirika kwake kudzakhala chishango chako ndi lihawo.
Sudzachita mantha ndi zoopsa za usiku,
    kapena muvi wowuluka masana,
kapena mliri umene umayenda mu mdima,
    kapena zowononga za pa nthawi ya masana.
Anthu 1,000 atha kufa pambali pako,
    anthu 10,000 kudzanja lako lamanja,
    koma zoopsazo sizidzafika pafupi ndi iwe.
Udzapenya ndi maso ako
    ndipo udzaona mmene anthu oyipa amalangidwira.

Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo;
    wavomera Yehova kukhala kothawira kwako.
10 Choncho palibe choyipa chimene chidzakugwera,
    zoopsa sizidzafika pafupi ndi tenti yako.
11 Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe,
    kuti akutchinjirize mosamala pa njira zako zonse;
12 ndipo adzakunyamula ndi manja awo,
    kuti phazi lako lisagunde pa mwala.
13 Udzapondaponda mkango ndi njoka,
    udzapondereza mkango wamphamvu ndiponso chinjoka.

14 “Chifukwa iye amandikonda,” akutero Yehova, “Ndidzamulanditsa;
    ndidzamuteteza pakuti wavomereza dzina langa.
15 Adzandiyitana, ndipo ndidzamuyankha;
    ndidzakhala naye pa mavuto,
    ndidzamupulumutsa ndi kumulemekeza.
16 Ndidzamupatsa moyo wautali
    ndi kumupulumutsa.”

Psalm 91

Whoever dwells in the shelter(A) of the Most High
    will rest in the shadow(B) of the Almighty.[a]
I will say of the Lord, “He is my refuge(C) and my fortress,(D)
    my God, in whom I trust.”

Surely he will save you
    from the fowler’s snare(E)
    and from the deadly pestilence.(F)
He will cover you with his feathers,
    and under his wings you will find refuge;(G)
    his faithfulness will be your shield(H) and rampart.
You will not fear(I) the terror of night,
    nor the arrow that flies by day,
nor the pestilence that stalks in the darkness,
    nor the plague that destroys at midday.
A thousand may fall at your side,
    ten thousand at your right hand,
    but it will not come near you.
You will only observe with your eyes
    and see the punishment of the wicked.(J)

If you say, “The Lord is my refuge,”
    and you make the Most High your dwelling,
10 no harm(K) will overtake you,
    no disaster will come near your tent.
11 For he will command his angels(L) concerning you
    to guard you in all your ways;(M)
12 they will lift you up in their hands,
    so that you will not strike your foot against a stone.(N)
13 You will tread on the lion and the cobra;
    you will trample the great lion and the serpent.(O)

14 “Because he[b] loves me,” says the Lord, “I will rescue him;
    I will protect him, for he acknowledges my name.
15 He will call on me, and I will answer him;
    I will be with him in trouble,
    I will deliver him and honor him.(P)
16 With long life(Q) I will satisfy him
    and show him my salvation.(R)

Footnotes

  1. Psalm 91:1 Hebrew Shaddai
  2. Psalm 91:14 That is, probably the king

91 He that dwelleth in the secret place of the most High shall abide under the shadow of the Almighty.

I will say of the Lord, He is my refuge and my fortress: my God; in him will I trust.

Surely he shall deliver thee from the snare of the fowler, and from the noisome pestilence.

He shall cover thee with his feathers, and under his wings shalt thou trust: his truth shall be thy shield and buckler.

Thou shalt not be afraid for the terror by night; nor for the arrow that flieth by day;

Nor for the pestilence that walketh in darkness; nor for the destruction that wasteth at noonday.

A thousand shall fall at thy side, and ten thousand at thy right hand; but it shall not come nigh thee.

Only with thine eyes shalt thou behold and see the reward of the wicked.

Because thou hast made the Lord, which is my refuge, even the most High, thy habitation;

10 There shall no evil befall thee, neither shall any plague come nigh thy dwelling.

11 For he shall give his angels charge over thee, to keep thee in all thy ways.

12 They shall bear thee up in their hands, lest thou dash thy foot against a stone.

13 Thou shalt tread upon the lion and adder: the young lion and the dragon shalt thou trample under feet.

14 Because he hath set his love upon me, therefore will I deliver him: I will set him on high, because he hath known my name.

15 He shall call upon me, and I will answer him: I will be with him in trouble; I will deliver him, and honour him.

16 With long life will I satisfy him, and shew him my salvation.