Add parallel Print Page Options

Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa. Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena. Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”

Mndandanda wa Anthu Oyamba Kubwera Kuchokera ku Ukapolo

Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe. Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:

Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake. Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana.

Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:

Zidzukulu za Parosi2,172
Zidzukulu za Sefatiya372
10 Zidzukulu za Ara652
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu)2,818
12 Zidzukulu za Elamu1,254
13 Zidzukulu za Zatu845
14 Zidzukulu za Zakai760
15 Zidzukulu za Binuyi648
16 Zidzukulu za Bebai628
17 Zidzukulu za Azigadi2,322
18 Zidzukulu za Adonikamu667
19 Zidzukulu za Abigivai2,067
20 Zidzukulu za Adini655
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya)98
22 Zidzukulu za Hasumu328
23 Zidzukulu za Bezayi324
24 Zidzukulu za Harifu112
25 Zidzukulu za Gibiyoni95.
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa188
27 Anthu a ku Anatoti128
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti42
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti743
30 Anthu a ku Rama ndi Geba621
31 Anthu a ku Mikimasi122
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai123
33 Anthu a ku Nebo winayo52
34 Ana a Elamu wina1,254
35 Zidzukulu za Harimu320
36 Zidzukulu za Yeriko345
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono721
38 Zidzukulu za Senaya3,930.

39 Ansembe anali awa:

A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa)973
40 Zidzukulu za Imeri1,052
41 Zidzukulu za Pasi-Huri1,247
42 Zidzukulu za Harimu1,017.

43 Alevi anali awa:

A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya74.

44 Anthu oyimba:

Zidzukulu za Asafu148.

45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa:

Zidzukulu za
Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai138.

46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa:

Zidzukulu za
Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.

57 Zidzukulu za antchito a Solomoni:

Zidzukulu za
Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu
zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo392.

61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.

62 Zidzukulu za
Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda642.

63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa:

zidzukulu za

Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).

64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo. 65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.

66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360. 67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245. 68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245. 69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.

70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530. 71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250. 72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.

73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo.

Ezara Awerenga Malamulo

Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.

After the wall had been rebuilt and I had set the doors in place, the gatekeepers,(A) the musicians(B) and the Levites(C) were appointed. I put in charge of Jerusalem my brother Hanani,(D) along with Hananiah(E) the commander of the citadel,(F) because he was a man of integrity and feared(G) God more than most people do. I said to them, “The gates of Jerusalem are not to be opened until the sun is hot. While the gatekeepers are still on duty, have them shut the doors and bar them. Also appoint residents of Jerusalem as guards, some at their posts and some near their own houses.”

The List of the Exiles Who Returned(H)

Now the city was large and spacious, but there were few people in it,(I) and the houses had not yet been rebuilt. So my God put it into my heart to assemble the nobles, the officials and the common people for registration by families. I found the genealogical record of those who had been the first to return. This is what I found written there:

These are the people of the province who came up from the captivity of the exiles(J) whom Nebuchadnezzar king of Babylon had taken captive (they returned to Jerusalem and Judah, each to his own town, in company with Zerubbabel,(K) Joshua, Nehemiah, Azariah, Raamiah, Nahamani, Mordecai, Bilshan, Mispereth, Bigvai, Nehum and Baanah):

The list of the men of Israel:

the descendants of Parosh2,172
of Shephatiah372
10 of Arah652
11 of Pahath-Moab (through the line of Jeshua and Joab)2,818
12 of Elam1,254
13 of Zattu845
14 of Zakkai760
15 of Binnui648
16 of Bebai628
17 of Azgad2,322
18 of Adonikam667
19 of Bigvai2,067
20 of Adin(L)655
21 of Ater (through Hezekiah)98
22 of Hashum328
23 of Bezai324
24 of Hariph112
25 of Gibeon95
26 the men of Bethlehem and Netophah(M)188
27 of Anathoth(N)128
28 of Beth Azmaveth42
29 of Kiriath Jearim, Kephirah(O) and Beeroth(P)743
30 of Ramah and Geba621
31 of Mikmash122
32 of Bethel and Ai(Q)123
33 of the other Nebo52
34 of the other Elam1,254
35 of Harim320
36 of Jericho(R)345
37 of Lod, Hadid and Ono(S)721
38 of Senaah3,930

39 The priests:

the descendants of Jedaiah (through the family of Jeshua)973
40 of Immer1,052
41 of Pashhur1,247
42 of Harim1,017

43 The Levites:

the descendants of Jeshua (through Kadmiel through the line of Hodaviah)74

44 The musicians:(T)

the descendants of Asaph148

45 The gatekeepers:(U)

the descendants of
Shallum, Ater, Talmon, Akkub, Hatita and Shobai138

46 The temple servants:(V)

the descendants of
Ziha, Hasupha, Tabbaoth,
47 Keros, Sia, Padon,
48 Lebana, Hagaba, Shalmai,
49 Hanan, Giddel, Gahar,
50 Reaiah, Rezin, Nekoda,
51 Gazzam, Uzza, Paseah,
52 Besai, Meunim, Nephusim,
53 Bakbuk, Hakupha, Harhur,
54 Bazluth, Mehida, Harsha,
55 Barkos, Sisera, Temah,
56 Neziah and Hatipha

57 The descendants of the servants of Solomon:

the descendants of
Sotai, Sophereth, Perida,
58 Jaala, Darkon, Giddel,
59 Shephatiah, Hattil,
Pokereth-Hazzebaim and Amon
60 The temple servants and the descendants of the servants of Solomon(W)392

61 The following came up from the towns of Tel Melah, Tel Harsha, Kerub, Addon and Immer, but they could not show that their families were descended from Israel:

62 the descendants of
Delaiah, Tobiah and Nekoda642

63 And from among the priests:

the descendants of
Hobaiah, Hakkoz and Barzillai (a man who had married a daughter of Barzillai the Gileadite and was called by that name).

64 These searched for their family records, but they could not find them and so were excluded from the priesthood as unclean. 65 The governor, therefore, ordered them not to eat any of the most sacred food until there should be a priest ministering with the Urim and Thummim.(X)

66 The whole company numbered 42,360, 67 besides their 7,337 male and female slaves; and they also had 245 male and female singers. 68 There were 736 horses, 245 mules,[a] 69 435 camels and 6,720 donkeys.

70 Some of the heads of the families contributed to the work. The governor gave to the treasury 1,000 darics[b] of gold, 50 bowls and 530 garments for priests. 71 Some of the heads of the families(Y) gave to the treasury for the work 20,000 darics[c] of gold and 2,200 minas[d] of silver. 72 The total given by the rest of the people was 20,000 darics of gold, 2,000 minas[e] of silver and 67 garments for priests.(Z)

73 The priests, the Levites, the gatekeepers, the musicians and the temple servants,(AA) along with certain of the people and the rest of the Israelites, settled in their own towns.(AB)

Ezra Reads the Law

When the seventh month came and the Israelites had settled in their towns,(AC)

Footnotes

  1. Nehemiah 7:68 Some Hebrew manuscripts (see also Ezra 2:66); most Hebrew manuscripts do not have this verse.
  2. Nehemiah 7:70 That is, about 19 pounds or about 8.4 kilograms
  3. Nehemiah 7:71 That is, about 375 pounds or about 170 kilograms; also in verse 72
  4. Nehemiah 7:71 That is, about 1 1/3 tons or about 1.2 metric tons
  5. Nehemiah 7:72 That is, about 1 1/4 tons or about 1.1 metric tons