Add parallel Print Page Options

Za Ufumu Wamtendere wa Mesiya

11 Padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese
    ndipo nthambi idzaphukira kuchokera ku mizu yake.
Mzimu wa Yehova udzakhala pa iye
    Mzimu wanzeru ndi wa kumvetsa zinthu,
    Mzimu wauphungu ndi wamphamvu,
    Mzimu wachidziwitso ndi wakuopa Yehova.
Ndipo kuopa Yehova ndiye chidzakhale chinthu chomukondweretsa.

Iye sadzaweruza potsata zooneka pamaso,
    kapena kugamula mlandu potsata zakumva;
koma amphawi adzawaweruza mwachilungamo,
    adzaweruza mwachilungamo mlandu wa anthu osauka a dziko lapansi.
Iye adzakantha dziko lapansi ndi mawu ake;
    atalamula Iyeyu anthu oyipa adzaphedwa.
Chilungamo chidzakhala ngati lamba wake
    ndipo kukhulupirika kudzakhala ngati chomangira mʼchiwuno mwake.

Mʼmbulu udzakhala pamodzi ndi mwana wankhosa,
    kambuku adzagona pansi pamodzi ndi mwana wambuzi,
mwana wangʼombe ndi mwana wa mkango adzadyera limodzi
    ndipo mwana wamngʼono adzaziweta.
Ngʼombe yayikazi ndi chimbalangondo zidzadya pamodzi,
    ana awo adzagona pamodzi,
    ndipo mkango udzadya udzu ngati ngʼombe.
Mwana wakhanda adzasewera pa dzenje la mamba,
    ndipo mwana wamngʼono adzapisa dzanja lake ku phanga la mphiri osalumidwa.
Sipadzakhala chilichonse chopweteka kapena chowononga
    pa phiri lopatulika la Yehova,
pakuti anthu a dziko lapansi adzadzaza ndi nzeru yotha kudziwa Yehova
    monga momwe nyanja imadzazira ndi madzi.

10 Tsiku limenelo mfumu yatsopano yochokera pa Muzu wa Yese idzakhala ngati chizindikiro kwa anthu a mitundu yonse. Mitundu ya anthu idzasonkhana kwa Iye, ndipo malo awo okhalapo adzakhala aulemerero. 11 Tsiku limenelo Ambuye adzatambasula dzanja lake kachiwiri kuti awombole anthu ake otsalira ku Asiriya, ku Igupto, ku Patirosi, Kusi, ku Elamu, ku Sinana, ku Hamati ndi pa zilumba za nyanja yamchere.

12 Adzakwezera mitundu ya anthu mbendera,
    ndipo adzasonkhanitsa otayika a ku Israeli;
Iye adzasonkhanitsa anthu obalalika a ku Yuda
    kuchokera ku mbali zonse zinayi za dziko lapansi.
13 Nsanje ya Efereimu idzatha,
    ndipo adani a Yuda adzatha;
Efereimu sadzachitira nsanje Yuda,
    ngakhale Yuda sadzamuda Efereimu.
14 Yuda ndi Efereimu adzathira nkhondo pa Afilisti mbali ya kumadzulo;
    ndipo onsewo pamodzi adzalanda zinthu za anthu a kummawa.
Adzalimbana ndi Edomu ndi Mowabu,
    ndipo Aamoni adzawagonjera.
15 Yehova adzaphwetsa
    mwendo wa nyanja ya Igupto;
adzatambasula dzanja lake ndipo adzawombetsa mphepo yotentha
    pa mtsinje wa Yufurate.
Iye adzawugawa mtsinjewo kukhala timitsinje tisanu ndi tiwiri
    kuti anthu athe kuwoloka powuma atavala nsapato.
16 Padzakhala msewu waukulu woti ayendepo anthu ake otsalira
    amene anatsalira ku Asiriya,
monga mmene panali msewu waukulu woyendapo Israeli
    pamene amachokera ku Igupto.

The Branch From Jesse

11 A shoot(A) will come up from the stump(B) of Jesse;(C)
    from his roots a Branch(D) will bear fruit.(E)
The Spirit(F) of the Lord will rest on him—
    the Spirit of wisdom(G) and of understanding,
    the Spirit of counsel and of might,(H)
    the Spirit of the knowledge and fear of the Lord
and he will delight in the fear(I) of the Lord.

He will not judge by what he sees with his eyes,(J)
    or decide by what he hears with his ears;(K)
but with righteousness(L) he will judge the needy,(M)
    with justice(N) he will give decisions for the poor(O) of the earth.
He will strike(P) the earth with the rod of his mouth;(Q)
    with the breath(R) of his lips he will slay the wicked.(S)
Righteousness will be his belt(T)
    and faithfulness(U) the sash around his waist.(V)

The wolf will live with the lamb,(W)
    the leopard will lie down with the goat,
the calf and the lion and the yearling[a] together;
    and a little child will lead them.
The cow will feed with the bear,
    their young will lie down together,
    and the lion will eat straw like the ox.(X)
The infant(Y) will play near the cobra’s den,
    and the young child will put its hand into the viper’s(Z) nest.
They will neither harm nor destroy(AA)
    on all my holy mountain,(AB)
for the earth(AC) will be filled with the knowledge(AD) of the Lord
    as the waters cover the sea.

10 In that day(AE) the Root of Jesse(AF) will stand as a banner(AG) for the peoples; the nations(AH) will rally to him,(AI) and his resting place(AJ) will be glorious.(AK) 11 In that day(AL) the Lord will reach out his hand a second time to reclaim the surviving remnant(AM) of his people from Assyria,(AN) from Lower Egypt, from Upper Egypt,(AO) from Cush,[b](AP) from Elam,(AQ) from Babylonia,[c] from Hamath(AR) and from the islands(AS) of the Mediterranean.(AT)

12 He will raise a banner(AU) for the nations
    and gather(AV) the exiles of Israel;(AW)
he will assemble the scattered people(AX) of Judah
    from the four quarters of the earth.(AY)
13 Ephraim’s jealousy will vanish,
    and Judah’s enemies[d] will be destroyed;
Ephraim will not be jealous of Judah,
    nor Judah hostile toward Ephraim.(AZ)
14 They will swoop down on the slopes of Philistia(BA) to the west;
    together they will plunder the people to the east.(BB)
They will subdue Edom(BC) and Moab,(BD)
    and the Ammonites(BE) will be subject to them.(BF)
15 The Lord will dry up(BG)
    the gulf of the Egyptian sea;
with a scorching wind(BH) he will sweep his hand(BI)
    over the Euphrates River.(BJ)
He will break it up into seven streams
    so that anyone can cross over in sandals.(BK)
16 There will be a highway(BL) for the remnant(BM) of his people
    that is left from Assyria,(BN)
as there was for Israel
    when they came up from Egypt.(BO)

Footnotes

  1. Isaiah 11:6 Hebrew; Septuagint lion will feed
  2. Isaiah 11:11 That is, the upper Nile region
  3. Isaiah 11:11 Hebrew Shinar
  4. Isaiah 11:13 Or hostility

11 And there shall come forth a rod out of the stem of Jesse, and a Branch shall grow out of his roots:

And the spirit of the Lord shall rest upon him, the spirit of wisdom and understanding, the spirit of counsel and might, the spirit of knowledge and of the fear of the Lord;

And shall make him of quick understanding in the fear of the Lord: and he shall not judge after the sight of his eyes, neither reprove after the hearing of his ears:

But with righteousness shall he judge the poor, and reprove with equity for the meek of the earth: and he shall smite the earth: with the rod of his mouth, and with the breath of his lips shall he slay the wicked.

And righteousness shall be the girdle of his loins, and faithfulness the girdle of his reins.

The wolf also shall dwell with the lamb, and the leopard shall lie down with the kid; and the calf and the young lion and the fatling together; and a little child shall lead them.

And the cow and the bear shall feed; their young ones shall lie down together: and the lion shall eat straw like the ox.

And the sucking child shall play on the hole of the asp, and the weaned child shall put his hand on the cockatrice' den.

They shall not hurt nor destroy in all my holy mountain: for the earth shall be full of the knowledge of the Lord, as the waters cover the sea.

10 And in that day there shall be a root of Jesse, which shall stand for an ensign of the people; to it shall the Gentiles seek: and his rest shall be glorious.

11 And it shall come to pass in that day, that the Lord shall set his hand again the second time to recover the remnant of his people, which shall be left, from Assyria, and from Egypt, and from Pathros, and from Cush, and from Elam, and from Shinar, and from Hamath, and from the islands of the sea.

12 And he shall set up an ensign for the nations, and shall assemble the outcasts of Israel, and gather together the dispersed of Judah from the four corners of the earth.

13 The envy also of Ephraim shall depart, and the adversaries of Judah shall be cut off: Ephraim shall not envy Judah, and Judah shall not vex Ephraim.

14 But they shall fly upon the shoulders of the Philistines toward the west; they shall spoil them of the east together: they shall lay their hand upon Edom and Moab; and the children of Ammon shall obey them.

15 And the Lord shall utterly destroy the tongue of the Egyptian sea; and with his mighty wind shall he shake his hand over the river, and shall smite it in the seven streams, and make men go over dryshod.

16 And there shall be an highway for the remnant of his people, which shall be left, from Assyria; like as it was to Israel in the day that he came up out of the land of Egypt.