Add parallel Print Page Options

16 Anthu a ku Mowabu
    atumiza mphatso za ana ankhosa onenepa,
kuchokera ku Sela kudutsa chipululu
    mpaka kukafika ku phiri la Ziyoni.
Monga momwe mbalame zimawulukira uku ndi uku
    akazimwaza mʼchisa,
momwemonso akazi a ku Mowabu
    akuyendayenda ku madooko a Arinoni.

Amowabu aja anawuza a ku Yuda kuti,
    “Tiwuzeni chochita, gamulani zoti tichite.
Inu mutiteteze kwa adani anthu.
    Mukhale ngati mthunzi wathu dzuwa lili pa liwombo.
Mutibise,
    musatipereke ife othawa nkhondo kwa adani athu.
Lolani kuti anthu othawa nkhondo a ku Mowabu azikhala pakati panu;
    mukhale populumukira pawo kwa wowonongayo.”

Nthawi idzafika ndipo wozunzayo sadzakhalaponso,
    kuwononga kudzaleka;
    waukaliyo adzachoka mʼdzikomo.
Mpando waufumu udzakhazikitsidwa mwachikondi;
    mmodzi mwa zidzukulu za Davide adzakhalapo mokhulupirika.
Iyeyo poweruza adzatsata chilungamo
    ndipo adzalimbikitsa kuchita zachilungamo.

Tinamva kuti Mowabu anadzikuza kwambiri.
    Kunyada kwawo
ndi kunyogodola kwawo ndi kudzitama kwawo,
    zonse ndi zopanda phindu.
Nʼchifukwa chake Amowabu akulira kwambiri;
    iwo akulirira dziko lawo.
Akubuma momvetsa chisoni
    chifukwa cha makeke a mphesa a ku Kiri Hareseti.
Minda ya ku Hesiboni yauma,
    minda ya mpesa ya ku Sibina yaguga.
Atsogoleri a mitundu ina anapondaponda
    minda ya mpesa wabwino,
imene nthambi zake zinakafika ku Yazeri,
    mpaka kutambalalira ku chipululu.
Mizu yake inakafika
    mpaka ku tsidya la nyanja.
Kotero Ine ndikulira, monga mmene akulirira anthu a ku Yazeri,
    chifukwa cha minda ya mpesa ya ku Sibima.
Inu anthu a ku Hesiboni, inu anthu a ku Eleali,
    ndikukunyowetsani ndi misozi!
Mwalephera kupeza zokolola,
    chifukwa cha nkhondo imene inawononga zokolola zonse.
10 Chimwemwe ndi chisangalalo zalekeka ku minda yanu ya zipatso;
    palibe amene akuyimba kapena kufuwula mʼminda ya mpesa;
palibe amene akupsinya vinyo ku malo opsinyira mphesa,
    pakuti ndathetsa kufuwula.
11 Chifukwa chake moyo wanga ukulira ngati pangwe kulirira Mowabu,
    mtima wanga ukubuwula chifukwa cha Kiri Hareseti.
12 Ngakhale anthu a ku Mowabu
    apite ku malo awo achipembedzo
koma amangodzitopetsa ndi kutaya nthawi chabe
    chifukwa sizidzatheka.

13 Awa ndi mawu amene Yehova wayankhula kale zokhudza Mowabu. 14 Koma tsopano Yehova akuti, “Zisanathe zaka zitatu, potsata mʼmene munthu waganyu amawerengera, ulemerero wa Mowabu udzakhala utatheratu ndipo anthu ake ambiri adzakhala atawonongeka, ndipo opulumuka ake adzakhala ochepa ndi ofowoka.”

16 Send lambs(A) as tribute(B)
    to the ruler of the land,
from Sela,(C) across the desert,
    to the mount of Daughter Zion.(D)
Like fluttering birds
    pushed from the nest,(E)
so are the women of Moab(F)
    at the fords(G) of the Arnon.(H)

“Make up your mind,” Moab says.
    “Render a decision.
Make your shadow like night—
    at high noon.
Hide the fugitives,(I)
    do not betray the refugees.
Let the Moabite fugitives stay with you;
    be their shelter(J) from the destroyer.”

The oppressor(K) will come to an end,
    and destruction will cease;(L)
    the aggressor will vanish from the land.
In love a throne(M) will be established;(N)
    in faithfulness a man will sit on it—
    one from the house[a] of David(O)
one who in judging seeks justice(P)
    and speeds the cause of righteousness.

We have heard of Moab’s(Q) pride(R)
    how great is her arrogance!—
of her conceit, her pride and her insolence;
    but her boasts are empty.
Therefore the Moabites wail,(S)
    they wail together for Moab.
Lament and grieve
    for the raisin cakes(T) of Kir Hareseth.(U)
The fields of Heshbon(V) wither,(W)
    the vines of Sibmah(X) also.
The rulers of the nations
    have trampled down the choicest vines,(Y)
which once reached Jazer(Z)
    and spread toward the desert.
Their shoots spread out(AA)
    and went as far as the sea.[b](AB)
So I weep,(AC) as Jazer weeps,
    for the vines of Sibmah.
Heshbon and Elealeh,(AD)
    I drench you with tears!(AE)
The shouts of joy(AF) over your ripened fruit
    and over your harvests(AG) have been stilled.
10 Joy and gladness are taken away from the orchards;(AH)
    no one sings or shouts(AI) in the vineyards;
no one treads(AJ) out wine at the presses,(AK)
    for I have put an end to the shouting.
11 My heart laments for Moab(AL) like a harp,(AM)
    my inmost being(AN) for Kir Hareseth.
12 When Moab appears at her high place,(AO)
    she only wears herself out;
when she goes to her shrine(AP) to pray,
    it is to no avail.(AQ)

13 This is the word the Lord has already spoken concerning Moab. 14 But now the Lord says: “Within three years,(AR) as a servant bound by contract(AS) would count them,(AT) Moab’s splendor and all her many people will be despised,(AU) and her survivors will be very few and feeble.”(AV)

Footnotes

  1. Isaiah 16:5 Hebrew tent
  2. Isaiah 16:8 Probably the Dead Sea

16 Send ye the lamb to the ruler of the land from Sela to the wilderness, unto the mount of the daughter of Zion.

For it shall be, that, as a wandering bird cast out of the nest, so the daughters of Moab shall be at the fords of Arnon.

Take counsel, execute judgment; make thy shadow as the night in the midst of the noonday; hide the outcasts; bewray not him that wandereth.

Let mine outcasts dwell with thee, Moab; be thou a covert to them from the face of the spoiler: for the extortioner is at an end, the spoiler ceaseth, the oppressors are consumed out of the land.

And in mercy shall the throne be established: and he shall sit upon it in truth in the tabernacle of David, judging, and seeking judgment, and hasting righteousness.

We have heard of the pride of Moab; he is very proud: even of his haughtiness, and his pride, and his wrath: but his lies shall not be so.

Therefore shall Moab howl for Moab, every one shall howl: for the foundations of Kirhareseth shall ye mourn; surely they are stricken.

For the fields of Heshbon languish, and the vine of Sibmah: the lords of the heathen have broken down the principal plants thereof, they are come even unto Jazer, they wandered through the wilderness: her branches are stretched out, they are gone over the sea.

Therefore I will bewail with the weeping of Jazer the vine of Sibmah: I will water thee with my tears, O Heshbon, and Elealeh: for the shouting for thy summer fruits and for thy harvest is fallen.

10 And gladness is taken away, and joy out of the plentiful field; and in the vineyards there shall be no singing, neither shall there be shouting: the treaders shall tread out no wine in their presses; I have made their vintage shouting to cease.

11 Wherefore my bowels shall sound like an harp for Moab, and mine inward parts for Kirharesh.

12 And it shall come to pass, when it is seen that Moab is weary on the high place, that he shall come to his sanctuary to pray; but he shall not prevail.

13 This is the word that the Lord hath spoken concerning Moab since that time.

14 But now the Lord hath spoken, saying, Within three years, as the years of an hireling, and the glory of Moab shall be contemned, with all that great multitude; and the remnant shall be very small and feeble.